Deuteronomy 22:9 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
M'munda wamphesa musabzalemo mbeu ina iliyonse. Ngati mutero, zonse zidzakhala zoletsedwa, mphesazo ndi mbeu zina zomwe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Musamabzala mbeu zosiyana m'munda wanu wamphesa, kuti zingaipsidwe mbeu zonse udazibzala, ndi zipatso za munda wamphesa zomwe.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Musadzale mbewu zamitundu iwiri mʼmunda wanu wa mpesa, ngati mutero, si mbewu zanu zokha zimene zidzakhale zodetsedwa, komanso zipatso za mʼmunda wamphesawo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Musamabzala mbeu zosiyana m'munda wanu wamphesa, kuti zingaipsidwe mbeu zonse udazibzala, ndi zipatso za munda wamphesa zomwe.