Deuteronomy 23:15 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kapolo akathaŵa kwa mbuye wake, nkubwera kwa inu kuti mumsunge, musambweze kwa mbuyakeyo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Musamapereka kwa mbuye wake kapolo wopulumuka kwa mbuye wake kuthawira kwa inu;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngati kapolo wathawa mbuye wake nakabisala kwanu, musamuperekenso kwa mbuye wakeyo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Musamapereka kwa mbuye wace kapolo wopulumuka kwa mbuye wace kuthawira kwa inu;