Deuteronomy 24:16 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Makolo asafere zolakwa za ana ao. Momwemonso ana asafere zolakwa za makolo ao. Munthu aphedwe chifukwa cha zoipa za iye mwini.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Atate asaphedwere ana, ndi ana asaphedwere atate; munthu yense aphedwere tchimo lakelake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Makolo asaphedwe chifukwa cha ana awo, ndipo ana asaphedwe chifukwa cha makolo awo, koma aliyense ayenera kufa chifukwa cha zolakwa zake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Atate asaphedwere ana, ndi ana asaphedwere atate; munthu yense aphedwere cimo lace lace.