Deuteronomy 25:10 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
M'dziko la Israele, banja la mwamunayo lidzatchedwa banja la munthu amene adamuvula nsapato yakumodzi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo azimutcha dzina lake m'Israele, Nyumba ya uje anamchotsa nsapato.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mbiri ya banja la munthu ameneyo idzadziwika mu Israeli kuti ndi Banja la Wovulidwa nsapato.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo azimucha dzina lace m'Israyeli, Nyumba ya uje anamcotsa nsapato.