Deuteronomy 25:11 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu aŵiri akamamenyana ndipo mkazi wa mmodzi pofuna kupulumutsa mwamuna wake, agwira mdani wakeyo ku moyo,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Akalimbana wina ndi mnzake, nakayandikiza mkazi wa winayo kulanditsa mwamuna wake m'dzanja la wompandayo, nakatulutsa dzanja lake, ndi kumgwira kudzivalo;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngati anthu awiri akuchita ndewu ndipo mkazi wa mmodzi wa iwo abwera kudzaleretsa mwamuna wake kwa mnzakeyo natambasula dzanja lake kugwira ku maliseche kwa winayo,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Akalimbana wina ndi mnzace, nakayandikiza mkazi wa winayo kulanditsa mwamuna wace m'dzanja la wompandayo, nakaturutsa dzanja lace, ndi kumgwira kudzibvalo;