Deuteronomy 25:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mwana woyamba kubadwa m'nyumbamo, adzakhala mwana wa mbale wake womwalirayo, kuti dzina la banja lake lisaferetu m'dziko la Israele.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo kudzali, kuti woyamba kubadwa amene adzambala, adzalowa dzina lake la mbale wake wakufayo, kuti dzina lake lisafafanizidwe m'Israele.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mwana wamwamuna woyamba amene mayiyo angabereke ayenera kutenga dzina la mwamuna wake womwalirayo kuti dzina lake lisafafanizike mu Israeli.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo kudzali, kuti woyamba kubadwa amene adzambala, adzalowa dzina lace la mbale wace wafayo, kuti dzina lace lisafafanizidwe m'Israyeli.