Deuteronomy 25:8 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamenepo akuluakulu amumzindamo amuitane kuti alankhule naye. Akapitirira ndithu kukana kumkwatira,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pamenepo akulu a mudzi wake amuitane, ndi kulankhula naye; ndipo akaimirira ndi kuti, Sindifuna kumtenga;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pamenepo akuluakulu a mu mzinda wawowo adzamuyitanitsa nakamba naye. Ngati alimbikirabe kunena kuti, “Ine sindikufuna kumukwatira mkaziyu,”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pamenepo akuru a mudzi wace amuitane, ndi kulankhula naye; ndipo akaimirira ndi kuti, Sindifuna kumtenga;