Deuteronomy 27:1 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pambuyo pake Mose, ali pamodzi ndi akuluakulu a Aisraele adauza anthu kuti, Muzimvera malamulo onse omwe ndikukupatsani leroŵa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Mose ndi akulu a Israele anauza anthu, nati, Sungani malamulo onse ndikuuzani lero.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mose ndi akuluakulu a Israeli analamula anthu kuti, “Sungani malamulo onse amene ndikukupatsani lero lino.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Mose ndi akuru a Israyeli anauza anthu, nati, Sungani malamulo onse ndikuuzani lero.