Deuteronomy 27:12 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mukangooloka Yordani, mafuko amene adzaima pa phiri la Gerizimu, pamene madalitso adzatchulidwa pa Aisraele, ndi aŵa: Simeoni, Levi, Yuda, Isakara, Yosefe ndi Benjamini.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Aimirire awa pa phiri la Gerizimu kudalitsa anthu, mutaoloka Yordani: Simeoni ndi Levi, ndi Yuda, ndi Isakara, ndi Yosefe, ndi Benjamini.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mukawoloka Yorodani, mafuko awa akayimirire pa Phiri la Gerizimu ndi kudalitsa anthu: Simeoni, Levi, Yuda, Isakara, Yosefe ndi Benjamini.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Aimirire awa pa phiri la Gerizimu kudalitsa anthu, mutaoloka Yordano: Simeoni ndi Levi, ndi Yuda, ndi Isakara, ndi Yosefe, ndi Benjamini.