Deuteronomy 27:13 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma mafuko ena amene adzaimirire pa phiri la Ebala, pamene matemberero adzatchulidwe pa Aisraele, ndi aŵa: Rubeni, Gadi, Asare, Zebuloni, Dani ndi Nafutali.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Naimirire awa pa phiri la Ebala, kutemberera: Rubeni, Gadi, ndi Asere, ndi Zebuloni, Dani ndi Nafutali.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo mafuko awa akayimirire pa Phiri la Ebala ndi kutchula matemberero: Rubeni, Gadi, Aseri, Zebuloni, Dani ndi Nafutali.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Naimirire awa pa phiri la Ebala, kutemberera: Rubeni, Gadi, ndi Aseri, ndi Zebuloni, Dani, ndi Nafitali.