Deuteronomy 27:2 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pa tsiku limene muzaoloke mtsinje wa Yordani ndi kuloŵa m'dziko limene Chauta, Mulungu wanu, akukupatsani, mudzaimiritse miyala yaitali, ndipo mudzaikulungize.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo kudzali, tsiku lakuoloka inu Yordani kulowa dziko limene Yehova Mulungu wanu akupatsani, kuti mudziutsire miyala yaikulu, ndi kuimata ndi njeresa;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mukawoloka mtsinje wa Yorodani kulowa mʼdziko limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani, muyimiritse miyala ingapo ikuluikulu ndi kuyikulungiza.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo kudzali, tsiku lakuoloka inu Yordano kulowa dziko limene Yehova Mulungu wanu akupatsani, kuti mudziutsire miyala yaikuru, ndi kuimata ndi njeresa;