Deuteronomy 32:33 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
ndi oipa kwambiri ngati vinyo wosanganiza ndi ululu wa njoka, ululu wopweteka wa mphiri.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Vinyo wao ndiwo ululu wa zinjoka, ndi ululu waukali wa mphiri.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Vinyo wawo ndi wa ululu wa njoka, ululu woopsa wa mphiri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Vinyo wao ndiwo ululu wa zinjoka, Ndi ululu waukali wa mphiri.