Deuteronomy 4:12 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chauta adalankhula nanu ali m'motomo, ndipo munkamumva akulankhula, koma osamuwona.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pamenepo Yehova ananena ndi inu ali pakati pa moto; munamva kunena kwa mau, osaona maonekedwe, koma kunenako.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kenaka Yehova anayankhula nanu kuchokera mʼmotowo. Inu munamva mawu ake okha koma simunamuone pakuti panali mawu chabe.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pamenepo Yehova ananena ndi inu ali pakati pa moto; munamva kunena kwa mau, osaona maonekedwe, koma kunenako.