Deuteronomy 4:21 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chauta, Mulungu wathu, adandikwiyira ine chifukwa cha inu. Ndipo adalumbira kuti ine sindiwoloka mtsinje wa Yordani kukaloŵa m'dziko lokoma limene akukupatsanilo ngati choloŵa chanu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Yehova anakwiyanso nane chifukwa cha mau anu, nalumbira kuti sindidzaoloka Yordani ine, ndi kuti sindidzalowa m'dziko lokomali Yehova Mulungu wanu akupatsani likhale cholowa chanu;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yehova anakwiya nane chifukwa cha inu, ndipo analumbira kwathunthu kuti sindidzawoloka Yorodani ndi kulowa mʼdziko labwinolo limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani inu ngati cholowa chanu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Yehova anakwiyanso nane cifukwa ca mau anu, nalumbira kuti sindidzaoloka Yordano ine, ndi kuti sindidzalowa m'dziko lokomali Yehova Mulungu wanu akupatsani likhale colowa canu;