Deuteronomy 4:24 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Paja Chauta, Mulungu wanu, ndi Mulungu wansanje, salola kuti wina apikisane naye. Ali ngati moto waukali.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti Yehova Mulungu wanu ndiye moto wonyeketsa, ndi Mulungu wansanje.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pakuti Yehova Mulungu wanu ndi moto wonyeketsa ndipo ndi Mulungu wansanje.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti Yehova Mulungu wanu ndiye moto wonyeketsa, ndi Mulungu wansanje.