Deuteronomy 4:26 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mukachita zimenezi, ndikukuuzani lero, kumwamba ndi dziko lapansi zikhale mboni, kuti simudzakhalitsa pa dziko. Mudzaonongeka m'dziko ili la patsidya pa Yordani, limene mukukakhalamolo. Mudzaonongeka nonsenu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndiitana kumwamba ndi dziko lapansi zichite mboni pa inu lero lino, kuti mudzaonongeka msangatu kuchotsedwa ku dziko limene muolokera Yordani kulilandira likhale lanulanu; masiku anu sadzachuluka pamenepo, koma mudzaonongeka konse.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
ine ndi kuti kumwamba ndi dziko lapansi zikhale mboni lero zokutsutsani kuti mudzawonongedwa msanga ndipo mudzachotsedwa mʼdziko limene mutenge mukawoloka Yorodani. Simudzakhalitsa kumeneko koma mudzawonongedwa ndithu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndiitana kumwamba ndi dziko lapansi zicite mboni pa inu lero lino, kuti mudzaonongeka msangatu kucotsedwa ku dziko limene muolokera Yordano kulilandira likhale lanu lanu; masiku anu sadzacuruka pamenepo, koma mudzaonongeka konse.