Deuteronomy 4:27 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chauta adzakumwazani pakati pa mitundu ina, ndipo oŵerengeka okha mwa inu ndiwo adzatsala pakati pa mitundu ina kumene Chauta adzakupirikitsirani.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Yehova adzakubalalitsani mwa mitundu ya anthu, nimudzatsala pang'ono mwa amitundu, kumene Yehova adzakutsogolerani kwao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yehova adzakubalalitsani pakati pa anthu ena. Ochepa okha pakati panu ndi amene adzapulumuke pakati pa anthu a mitundu ina kumene Yehova adzakupirikitsireniko.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Yehova adzakubalalitsani mwa mitundu ya anthu, nimudzatsala pang'ono mwa amitundu, kumene Yehova adzakutsogolerani kwao.