Deuteronomy 6:14 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Musamapembedza milungu ina, milungu imene amaipembedza anthu okhala mozunguliramu,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Musamatsata milungu ina, milungu ina ya mitundu ya anthu akuzinga inu;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Musamatsatire milungu ina, milungu ya anthu ena okuzungulirani,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Musamatsata milungu yina, milungu yina ya mitundu ya anthu akuzinga inu;