Deuteronomy 6:18 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Muzichita zokhazo zimene Chauta akuti ndi zolungama ndi zabwino, ndipo zinthu zidzakuyenderani bwino. Mudzalandira dziko labwinolo limene Chauta adalonjeza molumbira kuti adzapatsa makolo anu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo muzichita zolunjika ndi zokoma pamaso pa Yehova; kuti chikukomereni, ndi kuti mulowe kukalandira dziko lokomali Yehova analumbirira makolo anu,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Chitani zoyenera ndi zabwino pamaso pa Yehova, kuti zikuyendereni bwino ndi kuti mukhoza kukalowa ndi kulanda dziko labwinolo limene Yehova analonjeza molumbira kwa makolo anu,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo muzicita zolunjika ndi zokoma pamaso pa Yehova; kuti cikukomereni, ndi kuti mulowe kukalandira dziko lokomali Yehova analumbirira makolo anu,