Deuteronomy 6:20 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nthaŵi zakutsogoloko, ana anu adzakufunsani kuti, “Kodi chifukwa chiyani Chauta, Mulungu wathu, adakulamulani kuti muzimvera malamulo ndi malangizo ndi zina zonse zoyenera kuzitsatazi?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Akakufunsani ana anu m'tsogolomo, ndi kuti, Mbonizo, ndi malemba, ndi maweruzo, zimene Yehova Mulungu wathu anakulamulirani, zitani?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mʼtsogolo muno, ana anu akadzakufunsani kuti, “Kodi tanthauzo la ndondomeko, malangizo, zikhazikitso ndi malamulo amene Yehova Mulungu wathu anakulamulani nʼchiyani?”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Akakufunsani ana anu m'tsogolomo, ndi kuti, Mbonizo, ndi malemba, ndi maweruzo, zimene Yehova Mulungu wathu anakulamulirani, zitani?