Deuteronomy 6:21 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono inu mudzaŵauze kuti, “Ife tidaali akapolo a mfumu ya dziko la Ejipito, koma Mulungu adatipulumutsa ndi mphamvu zake zazikulu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pamenepo muzinena kwa ana anu, Tinali akapolo a Farao m'Ejipito; ndipo Yehova anatitulutsa m'Ejipito ndi dzanja lamphamvu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Inu mudzawawuze kuti, “Ife tinali akapolo a Farao ku Igupto, koma Yehova anatitulutsa ku Igupto ndi dzanja lamphamvu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pamenepo muzinena kwa ana anu, Tinali akapolo a Farao m'Aigupto; ndipo Yehova anatiturutsa m'Aigupto ndi dzanja lamphamvu.