Deuteronomy 6:23 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mulunguyo adatitulutsa ife ku Ejipito, natifikitsa kuno ndi kutipatsa dziko lino, monga momwe adalonjezera kwa makolo athu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndipo anatitulutsa komweko, kuti atilowetse, kutipatsa dzikoli analumbirira makolo athu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma anatitulutsa kumeneko ndi kutilowetsa kuno natipatsa dziko limene analonjeza mwa lumbiro kwa makolo athu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndipo anatiturutsa komweko, kuti atilowetse, kutipatsa dzikoli analumbirira makolo athu.