Deuteronomy 8:1 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Zonse zimene ndakulamulani lero, mumvere mokhulupirika, kuti mukhale ndi moyo, muchulukane, ndipo mukakhazikike m'dziko limene Chauta adalonjeza makolo anu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Muzisamalira kuchita malamulo onse amene ndikuuzani lero lino, kuti mukhale ndi moyo, ndi kuchuluka, ndi kulowa, ndi kulandira dziko limene Yehova analumbirira makolo anu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Samalani potsata lamulo lililonse limene ndikukupatsani lero, kuti mukhale ndi moyo ndi kuchulukana kuti mulande ndi kulowa mʼdziko limene Yehova analumbira kuti adzapereka kwa makolo anu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Muzisamalira kucita malamulo onse amene ndikuuzani lero lino, kuti mukhale ndi moyo, ndi kucuruka, ndi kulowa, ndi kulandira dziko limene Yehova analumbirira makolo anu.