Deuteronomy 8:10 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mudzakhala ndi chakudya chokwanira ndipo mudzakhuta, tsono mudzathokoza Chauta, Mulungu wanu, chifukwa wakupatsani dziko lokoma.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo mudzadya ndi kukhuta, ndi kuyamika Yehova Mulungu wanu chifukwa cha dziko lokomali anakupatsani.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mukadya ndi kukhuta, yamikani Yehova Mulungu wanu chifukwa cha dziko labwino limene wakupatsani.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo mudzadya ndi kukhuta, ndi kuyamika Yehova Mulungu wanu cifukwa ca dziko lokomali anakupatsani.