Deuteronomy 8:13 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
mukadzakhala ndi ng'ombe, nkhosa, siliva ndi golide, ndipo chuma chanu chikadzanka chiwonjezekeraonjezekera,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndipo zitachuluka ng'ombe zanu, ndi nkhosa zanu, zitachulukanso siliva wanu ndi golide wanu, zitachulukanso zonse muli nazo;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
ndi pamene ngʼombe zanu ndi nkhosa zanu zaswana, ndi siliva ndi golide wanu wachuluka ndiponso kuti zonse zimene muli nazo zachuluka,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndipo zitacuruka ng'ombe zanu, ndi nkhosa zanu, zitacurukanso siliva wanu ndi golidi wanu, zitacurukanso zonse muli nazo;