Deuteronomy 8:14 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
pamenepo musadzanyade ndi kuiŵala Chauta, Mulungu wanu, amene adakutulutsani ku Ejipito kumene mudaali akapolo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
mtima wanu ungatukumuke, nimungaiwale Yehova Mulungu wanu, amene anakutulutsani m'dziko la Ejipito, m'nyumba ya akapolo;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
mtima wanu udzayamba kunyada ndi kuyiwala Yehova Mulungu wanu, amene anakutulutsani ku Igupto, kukuchotsani ku dziko la ukapolo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
mtima wanu ungatukumuke, nimungaiwale Yehova Mulungu wanu, amene anakuturutsani m'dziko la Aigupto, m'nyumba ya akapolo;