Deuteronomy 8:19 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Musamuiŵale Chauta, Mulungu wanu, ndi kutembenukira kwa milungu ina kuti muipembedze. Mukachimwa motero, ndithudi mudzaonongeka.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo kudzakhala kuti mukaiwalatu Yehova Mulungu wanu, ndi kutsata milungu ina ndi kuitumikira, ndikuchitirani mboni lero lino kuti mudzaonongeka ndithu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ine ndine mboni yokutsutsani lero lino, kuti mukayiwala Yehova Mulungu wanu ndi kutsata milungu ina nʼkumayigwadira, mudzawonongeka ndithu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo kudzakhala kuti mukaiwalatu Yehova Mulungu wanu, ndi kutsata milungu yina ndi kuitumikira, ndikucitirani mboni lero lino kuti mudzaonongeka ndithu.