Deuteronomy 8:5 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Dziŵani kuti Chauta, Mulungu wanu, amakulangani monga momwe bambo amalangira ana ake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo muzindikire m'mtima mwanu, kuti monga munthu alanga mwana wake, momwemo Yehova Mulungu wanu akulangani inu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsono dziwani mu mtima mwanu kuti monga abambo amalanga mwana wawo, momwemonso Yehova Mulungu wanu amakulangani.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo muzindikire m'mtima mwanu, kuti monga munthu alanga mwana wace, momwemo Yehova Mulungu wanu akulangani inu.