Deuteronomy 9:25 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Motero ndidagwada pamaso pa Chauta ndipo ndidapemphera masiku makumi anai, usana ndi usiku, chifukwa Chauta adaatsimikiza zokuwonongani.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo ndinagwa pansi pamaso pa Yehova masiku makumi anai usana ndi usiku ndinagwa pansiwa; popeza Yehova adati kuti adzakuonongani.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ine ndinagwa chafufumimba pamaso pa Yehova kwa masiku makumi anayi usana ndi usiku chifukwa Yehova ananena kuti akuwonongani.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo ndinagwa pansi pamaso pa Yehova masiku makumi anai usana ndi usiku ndinagwa pansiwa; popeza Yehova adati kuti adzakuonongani.