Deuteronomy 9:29 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chonsecho anthu ameneŵa mudaŵasankha kuti akhale anuanu, ndipo mudaŵatulutsa ku Ejipito ndi mphamvu zanu zazikulu ndi mkono wanu wotambalitsa.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma iwo ndiwo anthu anu ndi cholowa chanu, amene mudatulutsa ndi mphamvu yanu yaikulu ndi dzanja lanu lotambasuka.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma iwowa ndi anthu anu, chuma chanu chimene munachitulutsa ndi mphamvu yanu yayikulu ndi mkono wanu wotambasuka.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma iwo ndiwo anthu anu ndi colowa canu, amene mudaturutsa ndi mphamvu yanu yaikuru ndi dzanja lanu lotambasuka.