Ecclesiastes 1:11 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Zakale sizikumbukika, ngakhale zinthu zimene zidzachitike pambuyo pake sizidzakumbukikanso ndi amene adzabwere m'tsogolo mwake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Zoyamba zija sizikumbukiridwa; ngakhale zomwe zilinkudzazo, omwe adzakhalabe m'tsogolomo, sadzazikumbukirai.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anthu akale sakumbukiridwa, ngakhale amene adzabwera mʼtsogolomu sadzakumbukiridwa ndi iwo amene adzabwere pambuyo pawo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Zoyamba zija sizikumbukiridwa; ngakhale zomwe zirinkudzazo, omwe adzakhalabe m'tsogolomo, sadzazikumbukirai.