Ecclesiastes 1:4 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mbadwo wina ukutha, wina ukudza, koma dziko lapansi limakhalapobe losasinthika.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mbadwo wina upita, mbadwo wina nufika; koma dziko lingokhalabe masiku onse.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mibado imabwera ndipo mibado imapita, koma dziko lapansi limakhalapobe nthawi zonse.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mbadwo wina opita, mbadwo wina nufika; koma dziko lingokhalabe masiku onse,