Ecclesiastes 10:16 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsoka kwa iwe dziko, ngati mfumu yako ikali mwana, ndipo nduna zako zimachezera madyerero usiku wonse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Tsoka kwa dzikowe, pamene mfumu yako ndiye mwana, ndipo akalonga ako adyera mamawa!
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsoka kwa iwe, iwe dziko ngati mfumu yako ikali mwana, ndipo atsogoleri ako amakhala pa madyerero mmamawa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Tsoka kwa dzikowe, pamene mfumu yako ndiye mwana, ndipo akalonga ako adyera mamawa!