Ecclesiastes 10:6 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Opusa amaŵapatsa ntchito zapamwamba, olemera nkumaŵapatsa ntchito zotsika.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
utsiru ukhazikika pamwamba penipeni, ndipo olemera angokhala mwamanyazi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Zitsiru amazipatsa ntchito zambiri zapamwamba, pamene anthu olemera amawapatsa ntchito zotsika.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
utsiru ukhazikika pamwamba penipeni, ndipo olemera angokhala mwamanyazi.