Ecclesiastes 10:7 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndaona akapolo akuyenda pa akavalo, m'menemo akalonga akuyenda pansi ngati akapolo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndaona akapolo atakwera pa akavalo, ndi mafumu, alikuyenda pansi ngati akopolo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndaona akapolo atakwera pa akavalo, pamene akalonga akuyenda pansi ngati akapolo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndaona akapolo atakwera pa akavalo, ndi mafumu, alikuyenda pansi ngati akapolo.