Ecclesiastes 11:7 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kuŵala kwam'maŵa kumasangalatsa, ndipo maso ako akaona dzuŵa amakondwa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Indetu kuunika nkokoma, maso napeza bwino m'kuona dzuwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kuwala nʼkwabwino, ndipo maso amasangalala kuona dzuwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Indetu kuunika nkokoma, maso napeza bwino m'kuona dzuwa.