Ecclesiastes 2:6 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndidaakumbanso maiŵe oti madzi ake azithirira minda ya mitengo yobzala ija.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndinadzipangira ndekha matamanda a madzi akuthirira madzi m'nkhalango momeramo mitengo;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndinakumba mayiwe osungiramo madzi woti ndizithirira minda ya mitengo yodzalidwa ija.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndinadzipangira ndekha matamanda a madzi akuthirira madzi m'nkhalango momeramo mitengo;