Ecclesiastes 3:10 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndaziwona ntchito zimene Mulungu adapatsa anthu kuti azizigwira.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndaona vuto limene Mulungu wapatsa ana a anthu kuti avutidwe nalo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ine ndinaona chipsinjo chimene Mulungu anayika pa anthu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndaona bvuto limene Mulungu wapatsa ana a anthu kuti abvutidwe nalo.