Ecclesiastes 4:2 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndinkaganiza kuti akufa aja amene adapita kale ndi amwai kwambiri kupambana amene akadali ndi moyo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo ndinatama akufa atatha kufa kupambana amoyo omwe alipobe;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo ndinanena kuti akufa, amene anafa kale, ndi osangalala kuposa amoyo, amene akanalibe ndi moyo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo ndinatama akufa atatha kufa kupambana amoyo omwe alipobe;