Ecclesiastes 4:5 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Paja akuti chitsiru chimangoti manja khodobala, nkumasoŵa chakudya mpaka kumafa ndi njala.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chitsiru chimanga manja ake, nichidya nyama yakeyake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Chitsiru chimangoti manja ake lobodo ndi kudzipha chokha ndi njala.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Citsiru cimanga manja ace, nicidya nyama yace yace.