Ecclesiastes 4:9 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kukhala aŵiri nkwabwino koposa kukhala wekha, chifukwa ntchito ya anthu aŵiri ili ndi phindu lopambana.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Awiri aposa mmodzi; pakuti ali ndi mphotho yabwino m'ntchito zao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kukhala awiri nʼkwabwino kuposa kukhala wekha, chifukwa ntchito ya anthu awiri ili ndi phindu:
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Awiri aposa mmodzi; pakuti ali ndi mphotho yabwino m'nchito zao.