Ecclesiastes 6:11 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mau akachuluka, zopandapake zimachulukanso. Nanga munthu apindulapo chiyani?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pokhala zinthu zambiri zingochulukitsa zachabe, kodi anthu aona phindu lanji?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mawu akachuluka zopandapake zimachulukanso, nanga munthu zimamupindulira chiyani?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pokhala zinthu zambiri zingocurukitsa zacabe, kodi anthu aona phindu lanji?