Ecclesiastes 6:4 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mtayo umangopita pachabe nkuloŵa mu mdima, ndipo umakaiŵalika mumdimamo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
pakuti ikudza mwachabe, nichoka mumdima, mdima nukwirira dzina lake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mtayo umangopita pachabe ndipo umapita mu mdima, ndipo mu mdimamo dzina lake limayiwalika.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
pakuti ikudza mwacabe, nicoka mumdima, mdima nukwirira dzina lace.