Ecclesiastes 6:5 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ngakhale mtayowo sudaone dzuŵa kapena kudziŵa kanthu kalikonse, komabe umapumula kupambana munthu wa moyo wautali uja,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ngakhale dzuwa siliona ngakhale kulidziwa, imeneyi ipambana winayo kupuma;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngakhale kuti mtayowo sunaone dzuwa kapena kudziwa kanthu kalikonse, koma umapumula kuposa munthu uja,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ngakhale dzuwa siliona ngakhale kulidziwa, imeneyi ipambana winayo kupuma;