Ecclesiastes 6:7 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu amagwira ntchito zolemetsa kuti apeze chakudya, komabe satha kukhutira kotheratu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ntchito zake zonse munthu angogwirira m'kamwa mwake, koma mtima wake sukhuta.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ntchito yonse ya munthu imathera pakamwa pake, komatu iye sakhutitsidwa ndi pangʼono pomwe.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Nchito zace zonse munthu angogwirira m'kamwa mwace, koma mtima wace sukhuta.