Ecclesiastes 7:16 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndiye usachite kunkitsa nako kulungama, kapena kunkitsa nazo nzeru. Nanga ufere ziti?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Usapambanitse kukhala wolungama; usakhale wanzeru koposa; bwanji ufuna kudziononga wekha?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Usakhale wolungama kwambiri kapena wanzeru kwambiri, udziwonongerenji wekha?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Usapambanitse kukhala wolungama; usakhale wanzeru koposa; bwanji ufuna kudziononga wekha?