Ecclesiastes 7:21 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Usamasamala zonse zokamba anthu, mwinamwina udzamva wantchito wako akukutukwana.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mau onsetu onenedwa usawalabadire; kuti usamve kapolo wako alikukutemberera;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Usamamvetsere mawu onse amene anthu amayankhula, mwina udzamva wantchito wako akukutukwana,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mau onsetu onenedwa usawalabadire; kuti usamve kapolo wako alikukutemberera;