Ecclesiastes 7:24 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Zimene zilipo zili kutali ndipo nzozama, kuzamatu kwambiri. Ndani angathe kuzidziŵa?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chakutali ndi chakuyadi, adzachipeza ndani?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nzeru zimene zilipo, zili kutali ndipo ndi zozama kwambiri, ndani angathe kuzidziwa?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cakutari ndi cakuyadi adzacipeza ndani?