Ecclesiastes 7:9 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Usamafulumira kukwiya, pakuti mkwiyo umakhalira zitsiru.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Usakangaze mumtima mwako kukwiya; pakuti mkwiyo ugona m'chifuwa cha zitsiru.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Usamafulumire kukwiya mu mtima mwako, pakuti mkwiyo ndi bwenzi la zitsiru.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Usakangaze mumtima mwako kukwiya; pakuti mkwiyo ugona m'cifuwa ca zitsiru.