Ecclesiastes 8:2 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Uzimvera lamulo la mfumu, ndipo chifukwa cha lumbiro lako kwa Mulungu usade nkhaŵa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Nditi, Sunga mau a mfumu, makamaka m'kulumbira Mulungu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ine ndikuti, mvera lamulo la mfumu, chifukwa unalumbira pamaso pa Mulungu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Nditi, Sunga mau a mfumu, makamaka m'kulumbira Mulungu.